by Jane Chinkwita
0 comments

Bungwe la atolankhani la media council of Malawi lachititsa maphunzilo a atolankhani ammene angagwirire ntchito munthawi ya zisankho.

Mkulu wa bungweli a Moses Kaufa wati atolankhani azidziwa malamulo ammene angawirire ntchito yawo mu nthawi ya zisankho.

AKaufa apempha atolankhani kulemba nkhani zoona zokhazokha komanso posatengera mbali pamnene tikuyandikira zisankho.

Iwo auza Atolankhani kuti azidziwa komwe angapite akachitidwa chipongwe.

Maphunzilowa amachitikira munzinda wa Blantyre ndi nthandizo la ndalama lochokera Ku National Commission For Unesco.

Wolemba Philadelphia Samera

You may also like

Leave a Comment

Neno FM is a non-profit and non-partisan community radio station established in October 2014 with a passion to assist the communities of Neno district and its surrounding districts to develop socially, economically in order to attain a level of poverty reduction through acquisition of information and education, relevant to social economic transformation.

Newsletter

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00